Wednesday 18 September 2013

Why Paul Mphwiyo was shot

Recently a well known Malawian economist was shot at his house in the capital Lilongwe. few days after his hospitalization three suspects were arrested of the involvement in the shooting of the top finance official but however in a strange way Malawi police is guarding the identities of the suspects and no-one knows why Paul Mphwiyo was shot.

Earlier this morning a source within government emailed this tip to this blog the email explains fully why Mphwiyo got shot:

muwelenge in confidence:I write to you coz you have shown courage to unmask these thugs, enafe to be very honest sitingakwanitse....
I am at the Ministry of Finance and I want to share with you what is being said in the corridors. You are free to publish this or leave it but if you chose to do so, then spare my name pliz coz ndiye kuti lots of things zoopsa can happen to me coz anthu akudziwa zoona koma akuopa. Choyamba ndi chakuti nkhani ya K120million ya Sithole ili related to this nkhani ya kuombeledwa kwa Paul Mphwiyo. Sithole ankagwila ntchito ku Accountant General ku Reconcilliation section and chifukwa chakuti ankapanga reconciliation for all the Ministries, anali ndi ma rights mu accounting system ya boma yotchedwa IFMIS mu ma Ministries onse. Chifukwa cha ichi and excitement anayamba ma deal. Chifukwa amayenela kupeza ma company otulutsila ndalama, iye amapanga approach anthu ambiri. Nkhaniyi itatchuka, Pika Manondo (yemwe ndi mnyamata wa Ralph Kasambara amamupezela tizibwenzi ndikumamuthamangilathamagila ngati Political Assistant) anamupeza Sithole ndikumupatsa ma Company names oti azipanga nawo deal. They have been stealing Governments funds for a long time and Pika Manondo (someone who was fired at Parliament for fraud has become so rich with K350million in the bank and owns a 15 vehicle car hire) since Ralph was appointed Minister. So these deals extended to Ralph Kasambara (also because anthuwa ankadziwa kuti one day they will need protection) and Wapona Kita. They used and also companies belonging to Maxwell Namata who was fired from Ministry of Housing due to fraud and Mr. Hophmally Makande's protégés. The Problem then arose about how they will be getting funds to fund Government Ministries which then can be used to process cheques to the Companies. That's when Ralph Kasambara approached Paul Mphwiyo as Budget Director ( coz it is the budget section in the Ministry of Finance that does the funding in the IFMIS system) to help with the deals. Paul Mphwiyo ndi wakuba kwambiri and its only a matter of time these investigations reveal this very fact. In actual fact, the Fortuner which was found at Sithole area 47 residence akuti belongs to Paul Mphwiyo. So , ma deal akhala akuyenda bwino bwino but of recent, Pika Manondo, Ralph Kambara, Hophmally Makande and Maxwell Namata (as owners of companies) were not happy ndi m'mene zinthu zimayendela, meaning kagawidwe ka ndalama. AND WHAT HAPPENENED IS THAT A WEEK BEFORE MWANA UYU SITHOLE KUGWIDWA, MBAVA ZA FUTI ZINAPITA KUNYUMBA KWAKE KWA SITHOLE NDIKUMUBELA K62Million (anazituma ndi achina Max, Pika ndi Ralph) THIS CAN BE VERIFIED WITH LINGADZI POLICE STATION (coz stupid enough, Stithole anakadandaula ku polisi kuti amubela ndalamazi). Ndichifukwa chake Wapona Kita rushed kukamuyimilila mulandu Sithole and that's why Ralph Kasambara was so concerned that he decided to go kwa Paul Mphwiyo and the Reserve Bank as Government cheques are effectively cleared through Reserve Bank of Malawi using Commercial Banks as agents. Paul Mphwiyo atamva izi anayamba makani kwambiri ndi kumawaopseza achina Pika, Maxwell Namata, Ralph and Hophmally kuti awaulula (akuti after all he was not the one who personally was effecting the fund in the IFMIS system but his Junior officer) UNLESS the thugs should return the money to Sithole. Apa ndi pamene zinthu zinafoyila kwambiri, kulusilana mpaka usiku wa tsiku lina Wapona Kita and Ralph Kasambara went to the house of Paul Mphwiyo to warn him that he could be killed because Maxwell Namata, Pika Manondo ndi achina Makande were not happy. THIS IS WHAT LED TO MPHWIYO'S shooting and PEOPLE KU MINISTRY OF FINANCE KNOW ABOUT THIS KWAMBIRI KWAKE As of today, 18th September, 2013 Pika Manondo is in South Africa and Maxwell Namata was in South Africa but connected to China.... rumour has it kuti they hired South Africans to kill Mphwiyo and I only hope he is safe in South Africa (kuti samuphako kumeneko) SO I JUST WANTED TO SHARE THIS BUT AS TO HOW YOU PUBLISH IT IS UP TO YOU OTHERWISE BECAREFUL COZ ANTHUWA NDi OWOPSA KWAMBIRI. THANKS

No comments:

Post a Comment